Machitidwe a Atumwi 7:36 - Buku Lopatulika36 Ameneyo anawatsogolera, natuluka nao atachita zozizwa ndi zizindikiro mu Ejipito, ndi mu Nyanja Yofiira, ndi m'chipululu zaka makumi anai. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201436 Ameneyo anawatsogolera, natuluka nao atachita zozizwa ndi zizindikiro m'Ejipito, ndi m'Nyanja Yofiira, ndi m'chipululu zaka makumi anai. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa36 Moseyo ndiye adaŵatsogolera anthuwo naŵatulutsa m'dziko la Ejipito. Ankachita zozizwitsa ndi zizindikiro ku Ejipito, pa Nyanja Yofiira, ndiponso m'chipululu zaka makumi anai. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero36 Iye anawatulutsa mu Igupto ndipo anachita zodabwitsa ndi zizindikiro zozizwitsa mu Igupto, pa Nyanja Yofiira, ndiponso mʼchipululu kwa zaka makumi anayi. Onani mutuwo |