Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Machitidwe a Atumwi 7:28 - Buku Lopatulika

28 Kodi ufuna kundipha ine, monga muja unapha Mwejipito dzulo?

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

28 Kodi ufuna kundipha ine, monga muja unapha Mwejipito dzulo?

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

28 Kodi ukufuna kuphanso ine monga udaphera Mwejipito dzulo lija?’

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

28 Kodi ukufuna kundipha monga momwe unaphera Mwigupto uja dzulo?’

Onani mutuwo Koperani




Machitidwe a Atumwi 7:28
3 Mawu Ofanana  

Koma anati, Wakuika iwe ndani ukhale mkulu ndi woweruza wathu? Kuteroku ukuti undiphe, monga unamupha Mwejipito? Ndipo Mose anachita mantha, nanena, Ndithu chinthuchi chadziwika.


Ndipo tinayembekeza ife kuti Iye ndiye wakudzayo kudzaombola Israele. Komatunso, pamodzi ndi izi zonse lero ndilo tsiku lachitatu kuyambira zidachitika izi.


Ndipo pakuona wina woti alikumchitira choipa, iye anamtchinjiriza, nambwezera chilango wozunzayo, nakantha Mwejipito.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa