Machitidwe a Atumwi 7:27 - Buku Lopatulika27 Koma iye wakumchitira mnzake choipa anamkankha, nati, Wakuika iwe ndani mkulu ndi wotiweruzira? Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201427 Koma iye wakumchitira mnzake choipa anamkankha, nati, Wakuika iwe ndani mkulu ndi wotiweruzira? Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa27 Koma amene adaaputa mnzakeyo adakankhira Mose kumbali nati, ‘Adakuika ndani kuti ukhale mkulu wathu ndi muweruzi wathu? Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero27 “Koma munthu amene amavutitsa mnzakeyo anakankha Mose ndipo anati, ‘Ndani anakuyika kuti ukhale wotilamulira ndi wotiweruza. Onani mutuwo |