Machitidwe a Atumwi 7:25 - Buku Lopatulika25 Ndipo anayesa kuti abale ake akazindikira kuti Mulungu alikuwapatsa chipulumutso mwa dzanja lake; koma sanazindikire. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201425 Ndipo anayesa kuti abale ake akazindikira kuti Mulungu alikuwapatsa chipulumutso mwa dzanja lake; koma sanazindikira. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa25 Iye ankaganiza kuti abale ake adzazindikira kuti Mulungu adamuika kuti adzaŵapulumutse, koma iwo sadazindikire. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero25 Mose anaganiza kuti abale ake adzazindikira kuti Mulungu anamuyika kuti awapulumutse koma iwo sanazindikire. Onani mutuwo |