Machitidwe a Atumwi 6:8 - Buku Lopatulika8 Ndipo Stefano, wodzala ndi chisomo ndi mphamvu, anachita zozizwa ndi zizindikiro zazikulu mwa anthu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20148 Ndipo Stefano, wodzala ndi chisomo ndi mphamvu, anachita zozizwa ndi zizindikiro zazikulu mwa anthu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa8 Stefano anali munthu amene Mulungu adamkomera mtima kwambiri namdzaza ndi mphamvu, kotero kuti ankachita zizindikiro zozizwitsa pakati pa anthu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero8 Stefano, munthu wodzazidwa ndi chisomo cha Mulungu ndi mphamvu anachita zodabwitsa ndiponso zizindikiro zazikulu pakati pa anthu. Onani mutuwo |