Machitidwe a Atumwi 6:6 - Buku Lopatulika6 amenewo anawaika pamaso pa atumwi; ndipo m'mene adapemphera, anaika manja pa iwo. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20146 amenewo anawaika pamaso pa atumwi; ndipo m'mene adapemphera, anaika manja pa iwo. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa6 Adaŵaimiritsa pamaso pa atumwi, ndipo atumwiwo adapemphera naŵasanjika manja. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero6 Iwo anapereka anthuwa kwa atumwi amene anawapempherera ndi kuwasanjika manja. Onani mutuwo |