Machitidwe a Atumwi 6:13 - Buku Lopatulika13 naimika mboni zonama, zakunena, Munthu ameneyo saleka kunenera malo oyera amene, ndi chilamulo; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201413 naimika mboni zonama, zakunena, Munthu ameneyo saleka kunenera malo oyera amene, ndi chilamulo; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa13 Adaimiritsa mboni zonama, izozo zidati, “Munthu uyu amangokhalira kulankhula mau onyoza Nyumba ya Mulungu ndiponso Malamulo a Mose. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero13 Iwo anabweretsa mboni zonama zimene zinati, “Munthu uyu akupitirirabe kuyankhula mawu onyoza malo oyera ndi malamulo. Onani mutuwo |