Machitidwe a Atumwi 6:12 - Buku Lopatulika12 Ndipo anautsa anthu, ndi akulu, ndi alembi, namfikira, namgwira iye, nadza naye kubwalo la akulu a milandu, Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201412 Ndipo anautsa anthu, ndi akulu, ndi alembi, namfikira, namgwira iye, nadza naye kubwalo la akulu, Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa12 Motero adautsa mitima ya anthu, ya akuluakulu ao, ndiponso ya aphunzitsi a Malamulo. Iwoŵa adamuukira Stefano, namgwira, nkupita naye ku Bungwe Lalikulu la Ayuda. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero12 Motero anawutsa mitima ya anthu, akulu ndi aphunzitsi amalamulo. Anamugwira Stefano ndi kumubweretsa ku Bwalo Lalikulu. Onani mutuwo |