Machitidwe a Atumwi 6:11 - Buku Lopatulika11 Pamenepo anafuna anthu akumpitira pansi, ndi kuti, Tidamumva iye alikunenera Mose ndi Mulungu mau amwano. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201411 Pamenepo anafuna anthu akumpitira pansi, ndi kuti, Tidamumva iye alikunenera Mose ndi Mulungu mau amwano. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa11 Tsono iwo adapangira anthu ena kuti azinena kuti, “Tidamumva akunyoza mwachipongwe Mose ndi Mulungu yemwe.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero11 Iwo ananyengerera anthu ena mwamseri kuti anene kuti, “Ife tinamva Stefano akuchitira chipongwe Mose ndiponso Mulungu.” Onani mutuwo |