Machitidwe a Atumwi 6:10 - Buku Lopatulika10 Ndipo sanathe kuipambana nzeru ndi Mzimu amene analankhula naye. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201410 Ndipo sanathe kuilaka nzeru ndi Mzimu amene analankhula naye. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa10 Koma adalephera kumgonjetsa, chifukwa iye ankalankhula ndi nzeru zochokera kwa Mzimu Woyera. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero10 Koma iwo sanathe kumugonjetsa chifukwa iye ankayankhula ndi nzeru zimene Mzimu Woyera anamupatsa. Onani mutuwo |