Machitidwe a Atumwi 5:39 - Buku Lopatulika39 koma ngati ichokera kwa Mulungu simungathe kuwapasula; kuti kapena mungapezeke otsutsana ndi Mulungu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201439 koma ngati ichokera kwa Mulungu simungathe kuwapasula; kuti kapena mungapezeke otsutsana ndi Mulungu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa39 Koma ngati nzochokera kwa Mulungu, inu simungathe kuŵaletsa ai. Mwina mungapezeke kuti mukulimbana ndi Mulungu.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero39 Koma ngati ndi zochokera kwa Mulungu inu simudzatha kuwaletsa anthu awa: inu mwina muzapezeka kuti mukulimbana ndi Mulungu.” Onani mutuwo |