Machitidwe a Atumwi 5:30 - Buku Lopatulika30 Mulungu wa makolo athu anaukitsa Yesu, amene munamupha inu, ndi kumpachika pamtengo. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201430 Mulungu wa makolo athu anaukitsa Yesu, amene munamupha inu, ndi kumpachika pamtengo. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa30 Mulungu wa makolo athu adaukitsa Yesu kwa akufa, Iye amene inu mudaamupha pakumpachika pa mtanda. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero30 Mulungu wa makolo athu anamuukitsa Yesu, amene inu munamupha pomupachika pa mtengo. Onani mutuwo |