Machitidwe a Atumwi 5:27 - Buku Lopatulika27 Ndipo m'mene adadza nao, anawaika pabwalo la akulu a milandu. Ndipo anawafunsa mkulu wa ansembe, Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201427 Ndipo m'mene adadza nao, anawaika pa bwalo la akulu. Ndipo anawafunsa mkulu wa ansembe, Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa27 Atafika nawo, adaŵakhazika pamaso pa Bungwe Lalikulu lija, ndipo mkulu wa ansembe onse adayamba kuŵafunsa mafunso. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero27 Atafika nawo atumwi aja, anawayimika pamaso pa Bwalo Lalikulu kuti afunsidwe mafunso ndi mkulu wa ansembe. Onani mutuwo |