Machitidwe a Atumwi 5:24 - Buku Lopatulika24 Koma m'mene anamva mau awa mdindo wa Kachisi ndi ansembe aakulu anathedwa nzeru ndi iwo aja, kuti ichi chidzatani. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201424 Koma m'mene anamva mau awa mdindo wa Kachisi ndi ansembe aakulu anathedwa nzeru ndi iwo aja, kuti ichi chidzatani. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa24 Pamene mkulu wa asilikali a ku Nyumba ya Mulungu ndi akulu a ansembe adamva mau ameneŵa, adatha nawo nzeru, osadziŵa kwachitika zotani. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero24 Mkulu wa alonda a Nyumba ya Mulungu ndi akulu a ansembe atamva zimenezi anathedwa nzeru, osadziwa kuti zimenezi zidzatha bwanji. Onani mutuwo |