Machitidwe a Atumwi 5:23 - Buku Lopatulika23 nanena, Nyumba yandende tinapeza chitsekere, ndi alonda alikuimirira pamakomo; koma pamene tinatsegula sitinapezamo mmodzi yense. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201423 nanena, Nyumba yandende tinapeza chitsekere, ndi alonda alikuimirira pamakomo; koma pamene tinatsegula sitinapezamo mmodzi yense. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa23 Adati, “Takapeza ndende ili chitsekere ndithu, ndipo alonda ali chilili pa makomo, koma titatsekula zitseko, sitidapezemo munthu.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero23 kuti, “Tinakapeza ndende ili chitsekere ndithu, ndi alonda atayimirira pa khomo, koma pamene tinatsekula zitseko, sitinapezemo munthu aliyense mʼkatimo.” Onani mutuwo |