Machitidwe a Atumwi 5:20 - Buku Lopatulika20 Pitani, ndipo imirirani, nimulankhule mu Kachisi kwa anthu onse mau a Moyo umene. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201420 Pitani, ndipo imirirani, nimulankhule m'Kachisi kwa anthu onse mau a Moyo umene. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa20 “Pitani m'Nyumba ya Mulungu muzikauza anthu mau onse okhudza za moyo watsopanowu.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero20 Mngeloyo anati, “Pitani, ku mabwalo a Nyumba ya Mulungu ndipo mukawuze anthu uthenga onse wamoyo watsopanowu.” Onani mutuwo |