Machitidwe a Atumwi 5:19 - Buku Lopatulika19 Koma mngelo wa Ambuye anatsegula pakhomo pa ndende usiku, nawatulutsa, nati, Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201419 Koma mngelo wa Ambuye anatsegula pakhomo pa ndende usiku, nawatulutsa, nati, Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa19 Koma usiku mngelo wa Ambuye adatsekula zitseko za ndendeyo naŵatulutsa. Adaŵauza kuti, Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero19 Koma usiku mngelo wa Ambuye anatsekula zitseko za ndende ndi kuwatulutsa Onani mutuwo |