Machitidwe a Atumwi 5:17 - Buku Lopatulika17 Koma anauka mkulu wa ansembe ndi onse amene anali naye, ndiwo a chipatuko cha Asaduki, nadukidwa, Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201417 Koma anauka mkulu wa ansembe ndi onse amene anali naye, ndiwo a chipatuko cha Asaduki, nadukidwa, Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa17 Pamenepo mkulu wa ansembe onse pamodzi ndi anzake aja, ndiye kuti a m'chipani cha Asaduki, onsewo adadukidwa nazo. Tsono adagamula zochitapo kanthu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero17 Koma mkulu wa ansembe pamodzi ndi onse omuthandiza, amene anali a gulu la Asaduki, anachita nsanje. Onani mutuwo |