Machitidwe a Atumwi 5:13 - Buku Lopatulika13 Koma palibe mmodzi wa otsalawo analimba mtima kuphatikana nao; komatu anthu anawakuzitsa; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201413 Koma palibe mmodzi wa otsalawo analimba mtima kuphatikana nao; komatu anthu anawakuzitsa; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa13 Mwa anthu enawo panalibe ndi mmodzi yemwe amene adaalimba mtima kuti azisonkhana nawo, komabe anthu onse ankaŵatama. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero13 Palibe ndi mmodzi yemwe analimba mtima kuphatikana nawo, ngakhale kuti anthu onse amawalemekeza kwambiri. Onani mutuwo |