Machitidwe a Atumwi 5:11 - Buku Lopatulika11 Ndipo anadza mantha aakulu pa Mpingo wonse, ndi pa onse akumva izi. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201411 Ndipo anadza mantha akulu pa Mpingo wonse, ndi pa onse akumva izi. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa11 Ndipo mpingo wonse ndi anthu onse amene adamva zimenezi, adagwidwa ndi mantha aakulu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero11 Mpingo wonse ndi anthu onse amene anamva zimenezi anachita mantha kwambiri. Onani mutuwo |