Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Machitidwe a Atumwi 4:37 - Buku Lopatulika

37 pokhala nao munda, anaugulitsa, nabwera nazo ndalama zake, naziika pa mapazi a atumwi.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

37 pokhala nao munda, anaugulitsa, nabwera nazo ndalama zake, naziika pa mapazi a atumwi.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

37 Nayenso adagulitsa munda wake, nabwera ndi ndalama zake kudzazipereka kwa atumwi.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

37 anagulitsa munda wake ndipo anadzapereka ndalamazo kwa atumwi.

Onani mutuwo Koperani




Machitidwe a Atumwi 4:37
4 Mawu Ofanana  

Ndipo onse amene adasiya nyumba, kapena abale, kapena alongo, kapena atate, kapena amai, kapena ana, kapena minda, chifukwa cha dzina langa, adzalandira zobwezeredwa zambirimbiri, nadzalowa moyo wosatha.


Ndipo onse akukhulupirira anali pamodzi, nakhala nazo zonse zodyerana.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa