Machitidwe a Atumwi 4:36 - Buku Lopatulika36 Ndipo Yosefe, wotchedwa ndi atumwi Barnabasi (ndilo losandulika mwana wa chisangalalo), Mlevi, fuko lake la ku Kipro, Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201436 Ndipo Yosefe, wotchedwa ndi atumwi Barnabasi (ndilo losandulika mwana wa chisangalalo), Mlevi, fuko lake la ku Kipro, Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa36 Panali munthu wina dzina lake Yosefe, wa fuko la Levi, mbadwa ya ku Kipro, amene atumwi adaamutcha Barnabasi, ndiye kuti Wolimbitsa mtima. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero36 Yosefe, wa fuko la Levi, wochokera ku Kupro amene atumwi anamutcha Barnaba, kutanthauza kuti mwana wachilimbikitso, Onani mutuwo |