Machitidwe a Atumwi 4:26 - Buku Lopatulika26 Anadzindandalitsa mafumu a dziko, ndipo oweruza anasonkhanidwa pamodzi, kutsutsana ndi Ambuye, ndi Khristu wake. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201426 Anadzindandalitsa mafumu a dziko, ndipo oweruza anasonkhanidwa pamodzi, kutsutsana ndi Ambuye, ndi Khristu wake. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa26 Mafumu a dziko lapansi adakonzekera, akulu a Boma adasonkhana pamodzi kulimbana ndi Chauta, ndiponso ndi wodzozedwa wake uja?’ Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero26 Mafumu a dziko lapansi akugwirizana nazo; ndipo olamulira asonkhana pamodzi kulimbana ndi Ambuye ndi wodzozedwa wakeyo.’ Onani mutuwo |