Machitidwe a Atumwi 4:22 - Buku Lopatulika22 Pakuti anali wa zaka zake zoposa makumi anai munthuyo, amene chizindikiro ichi chakumchiritsa chidachitidwa kwa iye. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201422 Pakuti anali wa zaka zake zoposa makumi anai munthuyo, amene chizindikiro ichi chakumchiritsa chidachitidwa kwa iye. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa22 Ndipo munthu wochiritsidwa mododometsayo anali wa zaka zopitirira makumi anai. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero22 Ndipo munthu amene anachiritsidwayo anali ndi zaka makumi anayi. Onani mutuwo |