Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Machitidwe a Atumwi 4:15 - Buku Lopatulika

15 Koma pamene anawalamulira iwo achoke m'bwalo la akulu a milandu, ananena wina ndi mnzake,

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

15 Koma pamene anawalamulira iwo achoke m'bwalo la akulu, ananena wina ndi mnzake,

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

15 Choncho adaŵalamula kuti atuluke m'bwalo la milandu lija, kenaka abwalowo adayamba kukambirana.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

15 Chifukwa chake anawalamula kuti atuluke mʼbwalo la milandu ndipo akulu abwalowo anayamba kukambirana.

Onani mutuwo Koperani




Machitidwe a Atumwi 4:15
4 Mawu Ofanana  

koma Ine ndinena kwa inu, kuti yense wokwiyira mbale wake wopanda chifukwa adzakhala wopalamula mlandu; ndipo amene adzanena ndi mbale wake, Wopanda pake iwe, adzakhala wopalamula mlandu wa akulu: koma amene adzati, Chitsiru iwe: adzakhala wopalamula Gehena wamoto.


Ndipotu pakuona munthu wochiritsidwayo alikuimirira pamodzi nao, analibe kanthu kakunena kotsutsa.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa