Machitidwe a Atumwi 4:14 - Buku Lopatulika14 Ndipotu pakuona munthu wochiritsidwayo alikuimirira pamodzi nao, analibe kanthu kakunena kotsutsa. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201414 Ndipotu pakuona munthu wochiritsidwayo alikuimirira pamodzi nao, analibe kanthu kakunena kotsutsa. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa14 Tsono poonanso munthu wochiritsidwa uja ataimirira pafupi ndi Petro ndi Yohane, adasoŵa poŵatsutsira. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero14 Koma popeza iwo amamuona munthu amene anachiritsidwa atayima pamodzi ndi iwo, palibe chimene akananena. Onani mutuwo |