Machitidwe a Atumwi 3:24 - Buku Lopatulika24 Koma angakhale aneneri onse kuyambira Samuele ndi akumtsatira, onse amene analankhula analalikira za masiku awa. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201424 Koma angakhale aneneri onse kuyambira Samuele ndi akumtsatira, onse amene analankhula analalikira za masiku awa. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa24 Ndipo aneneri onse amene adalankhula, kuyambira Samuele, mpaka onse amene adadza pambuyo pake, ankalalika za masiku omwe ano. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero24 “Ndipo aneneri onse ambiri amene anayankhula kuyambira Samueli, ananeneratu za masiku ano. Onani mutuwo |