Machitidwe a Atumwi 3:23 - Buku Lopatulika23 Ndipo kudzali, kuti wamoyo aliyense samvera mneneri ameneyu, adzasakazidwa konse mwa anthu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201423 Ndipo kudzali, kuti wamoyo aliyense samvera mneneri ameneyu, adzasakazidwa konse mwa anthu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa23 Aliyense amene sadzamvera Mneneriyo, amchotseretu mwa Aisraele ndi kumuwononga.’ Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero23 Aliyense amene sadzamvera mawu a mneneriyo, adzayenera kuchotsedwa pakati pa abale ake.’ Onani mutuwo |