Machitidwe a Atumwi 3:20 - Buku Lopatulika20 ndipo atume amene anaikidwa kwa inu, Khristu Yesu; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201420 ndipo atume amene anaikidwa kwa inu, Khristu Yesu; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa20 ndipo adzakutumizirani Yesu uja amene adamusankhuliratu kuti akhale Mpulumutsi wanu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero20 ndi kuti Iye atumize Yesu Khristu amene anasankhidwa chifukwa cha inu. Onani mutuwo |