Machitidwe a Atumwi 3:17 - Buku Lopatulika17 Ndipo tsopano, abale, ndidziwa kuti munachichita mosadziwa, monganso akulu anu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201417 Ndipo tsopano, abale, ndidziwa kuti munachichita mosadziwa, monganso akulu anu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa17 “Ndiponso tsopano abale anga, ndikudziŵa kuti inu ndi akuluakulu anu mudachita zimenezi mosadziŵa. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero17 “Tsopano abale ine ndikudziwa kuti inu munachita zimenezi mosadziwa, monga momwenso anachitira atsogoleri anu. Onani mutuwo |