Machitidwe a Atumwi 3:15 - Buku Lopatulika15 ndipo munamupha Mkulu wa moyo; amene Mulungu anamuukitsa kwa akufa; za ichi ife tili mboni. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201415 ndipo munamupha Mkulu wa moyo; amene Mulungu anamuukitsa kwa akufa; za ichi ife tili mboni. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa15 Mudapha Wopatsa moyo, koma Mulungu adamuukitsa kwa akufa. Ife ndife mboni za zimenezi. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero15 Inu munapha mwini moyo, koma Mulungu anamuukitsa kwa akufa. Ife ndife mboni za zimenezi. Onani mutuwo |