Machitidwe a Atumwi 3:11 - Buku Lopatulika11 Koma m'mene anagwira Petro ndi Yohane, anawathamangira pamodzi anthu onse kukhonde lotchedwa la Solomoni, alikudabwa ndithu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201411 Koma m'mene anagwira Petro ndi Yohane, anawathamangira pamodzi anthu onse kukhonde lotchedwa la Solomoni, alikudabwa ndithu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa11 Munthu uja adaakangamira Petro ndi Yohane, ndipo anthu onse adadabwa, naŵathamangira ku Khonde lotchedwa Khonde la Solomoni. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero11 Wopempha uja akuyenda pamodzi ndi Petro ndi Yohane, anthu onse anadabwa ndipo anawathamangira iwo kumalo wotchedwa Khonde la Solomoni. Onani mutuwo |