Machitidwe a Atumwi 28:9 - Buku Lopatulika9 Ndipo patachitika ichi, enanso a m'chisumbu, okhala nazo nthenda, anadza, nachiritsidwa; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20149 Ndipo patachitika ichi, enanso a m'chisumbu, okhala nazo nthenda, anadza, nachiritsidwa; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa9 Zitachitika zimenezi, anthu ena onse odwala pachilumbapo adabwera, Paulo nkuŵachiritsa. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero9 Zitachitika zimenezi, anthu onse odwala a pa chilumbacho anabwera ndipo anachiritsidwa. Onani mutuwo |