Machitidwe a Atumwi 28:7 - Buku Lopatulika7 Koma pafupi pamenepo panali minda, mwini wake ndiye mkulu chisumbucho, dzina lake Publio; amene anatilandira ife, natichereza okoma masiku atatu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20147 Koma pafupi pamenepo panali minda, mwini wake ndiye mkulu chisumbucho, dzina lake Publio; amene anatilandira ife, natichereza okoma masiku atatu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa7 Pafupi ndi malowo panali minda ya Publio, mkulu wa pachilumbapo. Iye adatilandira natisamala bwino masiku atatu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero7 Pafupi ndi malowa panali munda wa Popliyo, mkulu wa boma la pa chilumbacho. Iye anatilandira natisamala bwino masiku atatu. Onani mutuwo |