Machitidwe a Atumwi 28:3 - Buku Lopatulika3 Koma pamene Paulo adaola chisakata cha nkhuni, nachiika pamoto, inatulukamo njoka, chifukwa cha kutenthaku, niluma dzanja lake. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20143 Koma pamene Paulo adaola chisakata cha nkhuni, nachiika pamoto, inatulukamo njoka, chifukwa cha kutenthaku, niluma dzanja lake. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa3 Paulo adakatola nkhuni nabwerako ndi mtolo, ndipo pamene ankaziika pa moto, mumtolomo mudatuluka mphiri chifukwa cha kutenthako. Idamluma nkukanirira ku dzanja lakelo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero3 Paulo anatola mtolo wankhuni, pamene amayika pa moto, munatulukamo njoka chifukwa cha kutentha, ndipo inamuluma pa dzanja. Onani mutuwo |