Machitidwe a Atumwi 28:18 - Buku Lopatulika18 ndiwo, atandifunsafunsa ine anafuna kundimasula, popeza panalibe chifukwa cha kundiphera. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201418 ndiwo, atandifunsafunsa ine anafuna kundimasula, popeza panalibe chifukwa cha kundiphera. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa18 Iwo atandifunsa, adaafuna kundimasula, chifukwa sadapeze mlandu woyenera kundiphera. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero18 Iwo anandifufuza ndipo anafuna kundimasula chifukwa sanandipeze wopalamula mlandu woyenera kuphedwa. Onani mutuwo |