Machitidwe a Atumwi 27:8 - Buku Lopatulika8 ndipo popazapazapo movutika, tinafika kumalo ena dzina lake Pokocheza Pokoma; pafupi pamenepo panali mzinda wa Lasea. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20148 ndipo popazapazapo movutika, tinafika kumalo ena dzina lake Pokocheza Pokoma; pafupi pamenepo panali mudzi wa Lasea. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa8 Tidayenda movutikira m'mbali mwa chilumbacho, nkukafika ku malo ena otchedwa Madooko Okoma, pafupi ndi mzinda wa Lasea. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero8 Timayenda movutikira mʼmbali mwa chilumbacho ndipo tinafika pa malo wotchedwa Madooko Okoma, pafupi ndi mzinda wa Laseya. Onani mutuwo |