Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Machitidwe a Atumwi 27:39 - Buku Lopatulika

39 Ndipo kutacha sanazindikire dzikolo; koma anaona pali bondo la mchenga; kumeneko anafuna, ngati nkutheka, kuyendetsako ngalawa.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

39 Ndipo kutacha sanazindikira dzikolo; koma anaona pali bondo la mchenga; kumeneko anafuna, ngati nkutheka, kuyendetsako ngalawa.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

39 Kutacha, anthu sadazindikire mtundawo, koma adaona bondo la nyanja lamchenga. Tsono adaganiza kuti ngati nkotheka, akakocheze chombo kumeneko.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

39 Kutacha, anthu sanazindikire dzikolo, koma anaona pomwe sitima zimayimapo pamodzi ndi mchenga wa pa gombe. Iwo anaganiza zokocheza sitimayo kumeneko ngati zikanatheka kutero.

Onani mutuwo Koperani




Machitidwe a Atumwi 27:39
3 Mawu Ofanana  

Koma Yosefe, mwamuna wake, anali wolungama, ndiponso sanafune kunyazitsa iye, nayesa m'mtima kumleka iye m'tseri.


Ndipo m'mene anataya anangula anawasiya m'nyanja, namasulanso zingwe zomanga tsigiro; ndipo pokweza thanga la kulikulu, analunjikitsa kumchenga.


Ndipo titapulumuka, pamenepo tinadziwa kuti chisumbucho chinatchedwa Melita.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa