Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Machitidwe a Atumwi 27:36 - Buku Lopatulika

36 Ndipo anakhala olimbika mtima onse, natenga chakudya iwo omwe.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

36 Ndipo anakhala olimbika mtima onse, natenga chakudya iwo omwe.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

36 Pamenepo onse aja adalimba mtima, iwonso nkuyamba kudya.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

36 Onse analimba mtima nayamba kudyanso.

Onani mutuwo Koperani




Machitidwe a Atumwi 27:36
4 Mawu Ofanana  

Yembekeza Yehova, limbika, ndipo Iye adzalimbitsa mtima wako; inde, yembekeza Yehova.


Koma tsopano ndikuchenjezani mulimbike mtima; pakuti sadzatayika wamoyo mmodzi mwa inu, koma ngalawa ndiyo.


Chifukwa chake, limbikani mtima, amuna inu; pakuti ndikhulupirira Mulungu, kuti kudzatero monga momwe ananena ndi ine.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa