Machitidwe a Atumwi 27:34 - Buku Lopatulika34 Momwemo ndikuchenjezani mutenge kanthu kakudya; pakuti kumeneku ndi kwa chipulumutso chanu; pakuti silidzatayika tsitsi la pamutu wa mmodzi wa inu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201434 Momwemo ndikuchenjezani mutenge kanthu kakudya; pakuti kumeneku ndi kwa chipulumutso chanu; pakuti silidzatayika tsitsi la pa mutu wa mmodzi wa inu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa34 Ndikukupemphani tsono mudye kanthu kuti mupulumuke. Palibe ndi mmodzi yemwe mwa inu amene adzataye ngakhale tsitsi limodzi la kumutu kwake.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero34 Tsopano ine ndikukupemphani kuti mudye. Muyenera kudya kuti mupulumuke. Palibe ndi mmodzi yemwe wa inu adzataye ngakhale tsitsi limodzi la pamutu pake.” Onani mutuwo |