Machitidwe a Atumwi 27:32 - Buku Lopatulika32 Pamenepo asilikali anadula zingwe za bwato, naligwetsa. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201432 Pamenepo asilikali anadula zingwe za bwato, naligwetsa. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa32 Pamenepo asilikali aja adadula zingwe za kabwato kaja nakaleka kuti kagwe. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero32 Pamenepo asilikaliwo anadula zingwe za bwatolo ndipo linagwera mʼmadzi. Onani mutuwo |