Machitidwe a Atumwi 27:30 - Buku Lopatulika30 Ndipo m'mene amalinyero anafuna kuthawa m'ngalawa, natsitsira bwato m'nyanja, monga ngati anati aponye anangula kulikulu, Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201430 Ndipo m'mene amalinyero anafuna kuthawa m'ngalawa, natsitsira bwato m'nyanja, monga ngati anati aponye anangula kulikulu, Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa30 Antchito apachombo aja ankafuna kuthaŵamo m'chombo muja. Choncho adatsitsira kabwato kaja pa madzi, nachita ngati akufuna kutsitsira anangula m'nyanja kutsogolo kwa chombo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero30 Pofuna kuthawa mʼsitimayo, oyendetsa aja anatsitsira mʼnyanja bwato lopulumukiramo nʼkumachita ngati akufuna kutsitsira anangula mʼnyanjamo kutsogolo kwa sitimayo. Onani mutuwo |