Machitidwe a Atumwi 27:29 - Buku Lopatulika29 Ndipo pakuopa tingatayike pamiyala, anaponya anangula anai kumakaliro, nakhumba kuti kuche. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201429 Ndipo pakuopa tingatayike pamiyala, anaponya anangula anai kumakaliro, nakhumba kuti kuche. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa29 Poopa kuti chombo chingakatsakamire pa matanthwe, adatsitsira anangula anai m'nyanja kumbuyo kwa chombo. Kenaka ankangoyembekeza molakalaka kuti kuche. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero29 Poopa kuti tingagunde miyala, iwo anatsitsira anangula anayi mʼmadzi kumbuyo kwa sitimayo ndipo tinapemphera kuti kuche. Onani mutuwo |