Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Machitidwe a Atumwi 27:26 - Buku Lopatulika

26 Koma tiyenera kutayika pa chisumbu chakuti.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

26 Koma tiyenera kutayika pa chisumbu chakuti.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

26 Koma tidzatsakamira pa chilumba china.”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

26 Komabe tiyenera kukatsakamira pa chilumba china chake.”

Onani mutuwo Koperani




Machitidwe a Atumwi 27:26
4 Mawu Ofanana  

ndipo m'mene adaukweza, anachita nazo zothandizira, nakulunga ngalawa; ndipo pakuopa kuti angatayike pa Siriti, anatsitsa matanga, natengedwa motero.


Koma pofika usiku wakhumi ndi chinai, potengedwa ife kwina ndi kwina m'nyanja ya Adriya, pakati pa usiku amalinyero anazindikira kuti analikuyandikira kumtunda;


Ndipo pakuopa tingatayike pamiyala, anaponya anangula anai kumakaliro, nakhumba kuti kuche.


Ndipo titapulumuka, pamenepo tinadziwa kuti chisumbucho chinatchedwa Melita.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa