Machitidwe a Atumwi 27:25 - Buku Lopatulika25 Chifukwa chake, limbikani mtima, amuna inu; pakuti ndikhulupirira Mulungu, kuti kudzatero monga momwe ananena ndi ine. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201425 Chifukwa chake, limbikani mtima, amuna inu; pakuti ndikhulupirira Mulungu, kuti kudzatero monga momwe ananena ndi ine. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa25 Ndiye inu, limbani mtima, pakuti ndikukhulupirira Mulungu, kuti zimene wandiwuzazi zidzachitikadi momwemo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero25 Tsono limbani mtima, anthu inu, pakuti ine ndili ndi chikhulupiriro mwa Mulungu kuti zichitika monga momwe wandiwuzira. Onani mutuwo |