Machitidwe a Atumwi 27:23 - Buku Lopatulika23 Pakuti anaimirira kwa ine usiku walero mngelo wa Mulungu amene ndili wake, amenenso ndimtumikira, Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201423 Pakuti anaimirira kwa ine usiku walero mngelo wa Mulungu amene ndili wake, amenenso ndimtumikira, Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa23 Usiku womwe wathawu kunandibwerera mngelo wa Mulungu, Mulungu amene ine ndili wake, ndipo amene ndimamlemekeza. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero23 Usiku wathawu mngelo wa Mulungu, Mulungu amene ine ndili wake ndipo ndimamutumikira, anayima pafupi ndi ine, Onani mutuwo |