Machitidwe a Atumwi 27:22 - Buku Lopatulika22 Koma tsopano ndikuchenjezani mulimbike mtima; pakuti sadzatayika wamoyo mmodzi mwa inu, koma ngalawa ndiyo. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201422 Koma tsopano ndikuchenjezani mulimbike mtima; pakuti sadzatayika wamoyo mmodzi mwa inu, koma ngalawa ndiyo. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa22 Koma tsopano ndikukuuzani kuti mulimbe mtima, pakuti palibe ndi mmodzi yemwe mwa inu amene atayike, koma chombo chokha ndiye chiwonongeke. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero22 Koma tsopano ndikuti limbani mtima, chifukwa palibe aliyense wa inu amene adzataya moyo wake; koma sitima yokhayi idzawonongeka. Onani mutuwo |