Machitidwe a Atumwi 27:19 - Buku Lopatulika19 ndipo tsiku lachitatu anataya ndi manja ao a iwo eni zipangizo za ngalawa. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201419 ndipo tsiku lachitatu anataya ndi manja ao a iwo eni zipangizo za ngalawa. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa19 Ndipo pa tsiku lachitatu lake adataya m'nyanja ndi zipangizo za chombo zomwe. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero19 Pa tsiku lachitatu anaponya mʼnyanja zipangizo za mʼsitima ndi manja awo. Onani mutuwo |