Machitidwe a Atumwi 27:18 - Buku Lopatulika18 Ndipo povutika kwakukulu ndi namondweyo, m'mawa mwake anayamba kutaya akatundu; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201418 Ndipo povutika kwakukulu ndi namondweyo, m'mawa mwake anayamba kutaya akatundu; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa18 Popeza kuti tinkavutika naye kwambiri namondweyo, m'maŵa mwake adayamba kutaya katundu m'madzi. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero18 Ife tinavutika kwambiri ndi namondwe kotero kuti mmawa mwake tinayamba kuponya katundu mʼmadzi. Onani mutuwo |