Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Machitidwe a Atumwi 27:17 - Buku Lopatulika

17 ndipo m'mene adaukweza, anachita nazo zothandizira, nakulunga ngalawa; ndipo pakuopa kuti angatayike pa Siriti, anatsitsa matanga, natengedwa motero.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

17 ndipo m'mene adaukweza, anachita nazo zothandizira, nakulunga ngalawa; ndipo pakuopa kuti angatayike pa Siriti, anatsitsa matanga, natengedwa motero.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

17 Kenaka adakweza kabwatoko pa chombo, ndipo pambuyo pake adakulunga chombocho ndi zingwe kuti achilimbitse. Tsono poopa kuti angakagunde ku mchenga wa ku Siriti, adatsitsa mathanga nalola kungotengedwa ndi mphepo.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

17 Anthuwo atakweza bwatolo mʼsitima, anakulunga zingwe sitimayo kuti ayilimbitse. Poopa kuti angakagunde mchenga wa ku Surti, iwo anatsitsa nangula ndi kuyilola sitima kuti idzingoyenda ndi mphepo.

Onani mutuwo Koperani




Machitidwe a Atumwi 27:17
5 Mawu Ofanana  

Ndipo popita kuseri kwa chisumbu chaching'ono dzina lake Kauda, tinakhoza kumangitsa bwato koma movutika;


Koma tiyenera kutayika pa chisumbu chakuti.


Ndipo pakuopa tingatayike pamiyala, anaponya anangula anai kumakaliro, nakhumba kuti kuche.


Ndipo m'mene anataya anangula anawasiya m'nyanja, namasulanso zingwe zomanga tsigiro; ndipo pokweza thanga la kulikulu, analunjikitsa kumchenga.


Koma pofika pamalo pokomana mafunde awiri, anatsamitsapo ngalawa; ndipo kulikulu kunatsama, ndi kukhala kosasunthika, koma kumakaliro kunasweka ndi mphamvu ya mafunde.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa